Tsamba 32
Tsamba 32
Kodi n’zotheka kulankhula ndi amene amakhala kumwamba? ONANI TSAMBA 3-9.
Kodi ndi zoona kuti anthu otchulidwa m’Baibulo ankakhaladi ndi moyo zaka zambirimbiri? ONANI TSAMBA 12.
Kodi mayi wina anamva bwanji atagwira ntchito yothandiza anthu amene anavutika ndi chivomezi ku Haiti? ONANI TSAMBA 15.
Kodi inuyo mukanakhala kuti munalipo m’nthawi ya Yesu, mukanavomereza kuti iye ndi Mesiya? ONANI TSAMBA 18.
Kodi mungatani kuti muthandize makolo omwe sali pa banja? ONANI TSAMBA 22.