Ufumu wa Mulungu Wakwanitsa Zaka 100 Ndipo Ukulamulirabe

KOPERANI

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Padutsa Zaka 100 Tsopano

Padutsa zaka 100 tsopano kuchokera pamene filimu ya chilengedwe inayamba kuonetsedwa pofuna kuthandiza anthu kukhulupirira kuti Baibulo ndi Mawu a Mulungu.

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Sewero Limene Linathandiza Ambiri Kuphunzira Baibulo

Anthu ankatha kuonetsa chidule cha “Sewero la Pakanema la Chilengedwe” kumadera akutali ngakhale kumene kunalibe magetsi.

KALE LATHU

Kuulutsa Mawu a Uthenga Wabwino

Kodi a Mboni za Yehova ankachita zotani poulutsa Uthenga wa Ufumu kudzera pa wailesi ya WBBR?

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Galimoto Yodziwika Kwambiri Yokhala ndi Zokuzira Mawu

Kuchokera mu 1936 mpaka 1941, galimoto ya zokuzira mawu inathandiza a Mboni za Yehova ochepa a ku Brazil kuti athe kulalikira uthenga wa Ufumu kwa anthu ambiri m’dzikoli.