Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Obadiya

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Obadiya

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe mfundo zachidule za m’buku la Obadiya. Bukuli lili ndi uthenga wopereka chiyembekezo komanso limasonyeza kuti Yehova ndiye woyenera kulamulira.