Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

“Inu Yehova, ... Chikhulupiriro Changa Chili Mwa Inu”

Onerani vidiyoyi kuti muone mmene Hezekiya anasankhira zochita atakumana ndi mavuto ambiri. Iye anasonyeza kuti anali ndi chikhulupiriro cholimba komanso anali wokhulupirika. Hezekiya anali chitsanzo chabwino kwa Aisiraeli onse komanso ndi chitsanzo chabwino kwa anthu amene akutumikira Yehova masiku ano.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

BUKU LANGA LA NKHANI ZA BAIBULO

Mulungu Athandiza Mfumu Hezekiya

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Tsanzirani Anthu Amene Anali pa Ubwenzi Wolimba ndi Yehova

Kodi n’chiyani chinathandiza Rute, Hezekiya komanso Mariya kuti akhale pa ubwenzi wolimba ndi Mulungu?