TIMABUKU TOTHANDIZA ANTHU KUTIDZIWA BWINO PADZIKO LONSE
A Mboni za Yehova Komanso Mabuku ndi Zinthu Zina Zomwe Amapanga
Mabuku ndi zinthu zina zimene a Mboni za Yehova amapanga zimapezeka pa intaneti komanso zosindikiza. Zinthu zimenezi zimathandiza anthu kuyandikira Mulungu komanso kulimvetsa bwino Baibulo. Zimathandizanso kuti anthu asinthe miyoyo yawo n’kumakhala moyo wabwino.