Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kuona Malo ku Beteli

Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.

Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.

Ecuador

Sociedad de Estudiantes de la Biblia - Testigos de Jehová

Kilometer 23,5 via a la Costa (mamita 600 musanapeze maofesi olandirira misonkho)

GUAYAQUIL

ECUADOR

+593 4-371-2720

Kuona Malo

Lolemba mpaka Lachisanu

8:30 a.m. mpaka 10:30 a.m. ndi 1:30 p.m. mpaka 3:30 p.m.

Nthawi yonse: Ola limodzi ndi hafu

Zimene Timachita

Timayang’anira mipingo yoposa 900. Timamasulira mabuku ofotokoza nkhani za m’Baibulo m’Chikichuwa ndi zinenero zina zofanana nacho, komanso chinenero chamanja cha ku Ecuador ndi Chishuwa.

Koperani pepala losonyeza ofesi yathu.