Kuona Malo ku Beteli
Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.
Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.
Georgia
Aerodromis Dasahleba 13th Street, No. 10
TBILISI, 0182
GEORGIA
+995 32-276-23-59
Kuona Malo
Lolemba mpaka Lachisanu
8:30 a.m. mpaka 10:30 a.m. ndi 1:30 p.m. mpaka 3:30 p.m.
Nthawi yonse: Mphindi 30
Zimene Timachita
Timamasulira mabuku a nkhani za m’Baibulo m’Chiazebaijani, Chijojiya, Chisiriki cha Chikadishi. Timajambulanso mavidiyo ndi zinthu zina zomvetsera m’zinenero zina.