Pitani ku nkhani yake

Kuona Malo ku Beteli

Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.

Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.

Georgia

Aerodromis Dasahleba 13th Street, No. 10

TBILISI, 0182

GEORGIA

+995 32-276-23-59

Kuona Malo

Lolemba mpaka Lachisanu

8:30 a.m. mpaka 10:30 a.m. ndi 1:30 p.m. mpaka 3:30 p.m.

Nthawi yonse: Mphindi 30

Zimene Timachita

Timamasulira mabuku a nkhani za m’Baibulo m’Chiazebaijani, Chijojiya, Chisiriki cha Chikadishi. Timajambulanso mavidiyo ndi zinthu zina zomvetsera m’zinenero zina.

Koperani pepala losonyeza ofesi yathu.