Kuona Malo ku Beteli
Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.
Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.
Haiti
Santo 20, No. 9
Route de Croix-des-Bouquets
PORT-AU-PRINCE
HAITI
+509 2813-1560
+509 2813-1561
+509 2813-1562
+509 2513-3912
+509 2510-5163
Kuona Malo
Lolemba mpaka Lachisanu
8:00 a.m. mpaka 11:00 a.m. ndi 1:00 p.m. mpaka 4:00 p.m.
Nthawi yonse: Ola limodzi
Zimene Timachita
Timamasulira mabuku ofotokoza nkhani za m’Baibulo m’Chikiliyo cha ku Haiti. Timayang’anira ntchito imene mipingo yoposa 200 ya Mboni za Yehova ikugwira ku Haiti.