Kuona Malo ku Beteli
Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.
Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.
Kenya
Elgeyo Marakwet Rd
Kilimani area near Adams Arcade
NAIROBI
KENYA
+254 20-387-3211
+254 20-387-3212
+254 20-387-3213
Kuona Malo
Lolemba mpaka Lachisanu
8:00 a.m. mpaka 11:00 a.m. ndi 1:00 p.m. mpaka 4:00 p.m.
Nthawi yonse: Ola limodzi ndi hafu
Zimene Timachita
Timayang’anira ntchito yomasulira mabuku ofotokoza nkhani za m’Baibulo m’zinenero 10, kuphatikizapo Chinenero Chamanja cha ku Kenya. Timajambulanso mavidiyo ndi zinthu zina zomvetsera m’zinenero za ku Kenya. Timathandizira pa ntchito imene Mboni za Yehova zikugwira m’mayiko ena oyandikana ndi dziko la Kenya.