Kuona Malo ku Beteli
Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.
Kuyambiranso Kuona Malo: M'mayiko ambiri, anthu adzayambiranso kuona malo m'maofesi athu a nthambi kuyambira pa 1 June, 2023. Kuti mudziwe zambiri, lankhulani ndi abale a ku nthambi yomwe mukufuna kukaonayo. Komabe, musapite kukaona malo ngati mwapezeka ndi COVID-19 kapena ngati muli ndi zizindikiro za chimfine kapenanso ngati posachedwapa munakumana ndi munthu amene wapezeka ndi COVID-19.
Venezuela
Av. Intercomunal La Victoria-El Consejo
Frente a La Mora II
LA VICTORIA 2121 ESTADO ARAGUA
VENEZUELA
+58 244-400-5000
Kuona Malo
Lolemba mpaka Lachisanu
8:00 a.m. mpaka 11:00 a.m. ndi 1:00 p.m. mpaka 4:00 p.m.
Nthawi yonse: Ola limodzi
Zimene Timachita
Timamasulira mabuku ofotokoza nkhani za m’Baibulo m’Chinenero Chamanja cha ku Venezuela. Mwezi uliwonse, timatumiza kumipingo mabuku olemera matani 27 a m’zinenero 29. Timayang’anira ntchito imene Mboni za Yehova zoposa 125,000 zikugwira ku Venezuela.