Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Anzathu Atsopano ku Warwick

Anzathu Atsopano ku Warwick

Akuluakulu a tawuni ya Warwick ndi enanso akufotokoza zinthu zabwino zimene zakhala zikuchitika pamene ankagwira ntchito ndi a Mboni za Yehova pomanga likulu lawo latsopano.