Malo a Nkhani
‘Ndikufunitsitsa Kudzaona Boma Litachotsa Chiletso Chomwe Linaikira a Mboni za Yehova’
Zaka zambirimbiri m’mbuyomo, a Mboni za Yehova ankapembedza mwaufulu ku Egypt. Nyuzi ina ya paintaneti inafotokoza kuti kuchokera nthawi imeneyo a Mboni za Yehova akhala akusonyeza makhalidwe abwino ngakhale kuti akhala akuzunzidwa kwa zaka zambiri.
Dziko la South Korea Likuchitira a Dong-hyuk Shin Zinthu Zopanda Chilungamo
Ufulu wa a Shin wochita zinthu mogwirizana ndi chikumbumtima chawo komanso chipembedzo chawo ukuphwanyidwa powalanga mopanda chilungamo chifukwa chokana kuchita maphunziro a ntchito ya usilikali.
A Mboni Anapatsidwa Mphotho Yapamwamba Chifukwa Chogwiritsa Ntchito Njira Zamakono Pomanga Nthambi Yawo Yatsopano ku Britain
A Mboni za Yehova ku analandira mphoto yapamwamba chifukwa cha mmene anamangira nthambi yawo yatsopano ku Britain komanso chifukwa chogwiritsa ntchito njira zatsopano zoteteza chilengedwe pa ntchitoyi.
A Mboni za Yehova Akutonthoza Anthu Omwe Anakhudzidwa ndi Zauchifwamba ku Turku, Finland
Zimene ofesi ya nthambi inachita pothandiza mwamsanga anthu amene anakhudzidwa ndi zauchifwambazi zinathandiza kwambiri a Mboni komanso ena omwe si a Mboni.
Makhoti a ku Germany Amaona Misonkhano Ikuluikulu ya Mboni za Yehova Monga Maholide Achipembedzo
Misonkhano ya chigawo ya a Mboni tsopano imaonedwa monga maholide a chipembedzo, ndipo zimenezi zikusonyeza ufulu umene makolo ali nawo wophunzitsa ana awo zinthu zimene amakhulupirira.
A Mboni za Yehova ndi Okonzeka Kuyamba Ntchito Yomanganso Nyumba Zoonongeka ndi Chivomezi ku Guatemala ndi ku Mexico
A Mboni za Yehova ayamba ntchito yayikulu yothandiza a Mboni anzawo a ku Mexico ndi ku Guatemala amene anakhudzidwa ndi zivomezi ziwiri zomwe zinaononga kwambiri.