Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Malo a Nkhani

 

2017-09-21

EGYPT

‘Ndikufunitsitsa Kudzaona Boma Litachotsa Chiletso Chomwe Linaikira a Mboni za Yehova’

Zaka zambirimbiri m’mbuyomo, a Mboni za Yehova ankapembedza mwaufulu ku Egypt. Nyuzi ina ya paintaneti inafotokoza kuti kuchokera nthawi imeneyo a Mboni za Yehova akhala akusonyeza makhalidwe abwino ngakhale kuti akhala akuzunzidwa kwa zaka zambiri.

2018-08-29

SOUTH KOREA

Dziko la South Korea Likuchitira a Dong-hyuk Shin Zinthu Zopanda Chilungamo

Ufulu wa a Shin wochita zinthu mogwirizana ndi chikumbumtima chawo komanso chipembedzo chawo ukuphwanyidwa powalanga mopanda chilungamo chifukwa chokana kuchita maphunziro a ntchito ya usilikali.

2017-11-23

UNITED KINGDOM

A Mboni Anapatsidwa Mphotho Yapamwamba Chifukwa Chogwiritsa Ntchito Njira Zamakono Pomanga Nthambi Yawo Yatsopano ku Britain

A Mboni za Yehova ku analandira mphoto yapamwamba chifukwa cha mmene anamangira nthambi yawo yatsopano ku Britain komanso chifukwa chogwiritsa ntchito njira zatsopano zoteteza chilengedwe pa ntchitoyi.

2017-12-26

FINLAND

A Mboni za Yehova Akutonthoza Anthu Omwe Anakhudzidwa ndi Zauchifwamba ku Turku, Finland

Zimene ofesi ya nthambi inachita pothandiza mwamsanga anthu amene anakhudzidwa ndi zauchifwambazi zinathandiza kwambiri a Mboni komanso ena omwe si a Mboni.

2017-10-11

GERMANY

Makhoti a ku Germany Amaona Misonkhano Ikuluikulu ya Mboni za Yehova Monga Maholide Achipembedzo

Misonkhano ya chigawo ya a Mboni tsopano imaonedwa monga maholide a chipembedzo, ndipo zimenezi zikusonyeza ufulu umene makolo ali nawo wophunzitsa ana awo zinthu zimene amakhulupirira.

2018-02-06

MEXICO

A Mboni za Yehova ndi Okonzeka Kuyamba Ntchito Yomanganso Nyumba Zoonongeka ndi Chivomezi ku Guatemala ndi ku Mexico

A Mboni za Yehova ayamba ntchito yayikulu yothandiza a Mboni anzawo a ku Mexico ndi ku Guatemala amene anakhudzidwa ndi zivomezi ziwiri zomwe zinaononga kwambiri.