Pitani ku nkhani yake

MAY 12, 2014
NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Akatswiri Akufotokoza Zokhudza Ufulu Umene Munthu Ali Nawo, Wokana Kulowa Usilikali

Akatswiri Akufotokoza Zokhudza Ufulu Umene Munthu Ali Nawo, Wokana Kulowa Usilikali

Akatswiri odziwa za ufulu wachibadwidwe ku Ulaya akukambirana nkhani yokhudza kukana kulowa usilikali, yomwe ikukhudzana ndi ufulu wachibadwidwe umene munthu aliyense ali nawo.

  • Bambo Nils Muiznieks omwe ndi Mkulu wa Bungwe Loona za Ufulu Wachibadwidwe wa anthu a m’mayiko a ku Ulaya, Bungweli linakhazikitsidwa kuti lizilimbikitsa  mayiko amene ali m’bungweli  kuti azilemekeza ufulu wa anthu.

  • Bambo Richard Clayton QC ndi oimira dziko la United Kingdom mu komiti yoona za malamulo ya Bungwe la mayiko a ku Ulaya.

Onerani zimene akatswiriwa ananena.