Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Russia

 

2017-04-06

RUSSIA

Vasiliy Kalin: Zimene Woimira a Mboni Anayankhula Boma la Russia Litaopseza Kuti Liletsa Ntchito ya Mboni za Yehova M’dzikolo

Woimira Likulu la Mboni za Yehova m’dziko la Russia, a Vasiliy Kalin, akupempha akuluakulu a boma kuti asiye kuzunza a Mboni za Yehova popanda chifukwa.

2017-02-07

RUSSIA

Zimene Akatswiri Ena Ananena: Dziko la Russia Likugwiritsa Ntchito Molakwika Lamulo Loteteza Anthu ku Zinthu Zoopsa Pofuna Kuletsa Ntchito ya Mboni za Yehova

Iyi ndi nkhani yoyamba pa nkhani zitatu zochokera pa zimene a katswiri pa nkhani ya zipembedzo, ndale, chikhalidwe komanso akatswiri a ulamuliro wa Soviet ananena.

2016-07-08

RUSSIA

Zimene Dziko la Russia Likuchita Pofuna Kutseka Likulu la Mboni za Yehova Zikusokoneza Ufulu Wawo Wolambira Mulungu Momasuka

A Mboni m’dziko la Russia akhoza kukhala ndi ufulu wokhulupirira zimene akufuna koma osakhala ndi ufulu wochita zinthu zokhudza chipembedzo chawo.

2016-05-17

RUSSIA

Akuluakulu a Boma la Russia Akufuna Kutseka Likulu la Mboni za Yehova M’dzikolo

Kalata imene akuluakulu a boma la Russia alemba posachedwapa ikusonyeza kuti bomali likufuna kuletsa a Mboni kupembedza.

2016-05-17

RUSSIA

Komiti Ina ya Bungwe la United Nations Yanena Kuti Dziko la Russia Likugwiritsa Ntchito Lamulo Loteteza Anthu ku Zinthu Zoopsa Polimbana ndi a Mboni

Komiti Ina ya Bungwe la United Nations Yanena Kuti Dziko la Russia Likugwiritsa Ntchito Lamulo Loteteza Anthu ku Zinthu Zoopsa Polimbana ndi a Mboni

2016-03-04

RUSSIA

Khoti la Taganrog Linapereka Chilango kwa a Mboni Chifukwa Chochita Zachipembedzo

A Mboni onse 16 anapezeka kuti ndi olakwa pa mlandu wochita zinthu zoopsa zobweretsa chisokonezo. Chigamulochi chikhoza kuchititsa kuti a Mboni am’madera ambiri ku Russia aziimbidwa mlandu chifukwa chochita zachipembedzo.