Russia
Vasiliy Kalin: Zimene Woimira a Mboni Anayankhula Boma la Russia Litaopseza Kuti Liletsa Ntchito ya Mboni za Yehova M’dzikolo
Woimira Likulu la Mboni za Yehova m’dziko la Russia, a Vasiliy Kalin, akupempha akuluakulu a boma kuti asiye kuzunza a Mboni za Yehova popanda chifukwa.
Zimene Akatswiri Ena Ananena: Dziko la Russia Likugwiritsa Ntchito Molakwika Lamulo Loteteza Anthu ku Zinthu Zoopsa Pofuna Kuletsa Ntchito ya Mboni za Yehova
Iyi ndi nkhani yoyamba pa nkhani zitatu zochokera pa zimene a katswiri pa nkhani ya zipembedzo, ndale, chikhalidwe komanso akatswiri a ulamuliro wa Soviet ananena.
Zimene Dziko la Russia Likuchita Pofuna Kutseka Likulu la Mboni za Yehova Zikusokoneza Ufulu Wawo Wolambira Mulungu Momasuka
A Mboni m’dziko la Russia akhoza kukhala ndi ufulu wokhulupirira zimene akufuna koma osakhala ndi ufulu wochita zinthu zokhudza chipembedzo chawo.
Akuluakulu a Boma la Russia Akufuna Kutseka Likulu la Mboni za Yehova M’dzikolo
Kalata imene akuluakulu a boma la Russia alemba posachedwapa ikusonyeza kuti bomali likufuna kuletsa a Mboni kupembedza.
Komiti Ina ya Bungwe la United Nations Yanena Kuti Dziko la Russia Likugwiritsa Ntchito Lamulo Loteteza Anthu ku Zinthu Zoopsa Polimbana ndi a Mboni
Komiti Ina ya Bungwe la United Nations Yanena Kuti Dziko la Russia Likugwiritsa Ntchito Lamulo Loteteza Anthu ku Zinthu Zoopsa Polimbana ndi a Mboni
Khoti la Taganrog Linapereka Chilango kwa a Mboni Chifukwa Chochita Zachipembedzo
A Mboni onse 16 anapezeka kuti ndi olakwa pa mlandu wochita zinthu zoopsa zobweretsa chisokonezo. Chigamulochi chikhoza kuchititsa kuti a Mboni am’madera ambiri ku Russia aziimbidwa mlandu chifukwa chochita zachipembedzo.