Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kuchita Chibwenzi

Kulikonse kumene mungapite, mumaona anthu omwe ali pa chibwenzi. Kodi inuyo ndi okonzeka kukhala pa chibwenzi? Ngati ndi choncho, mungatani kuti mupewe kulakwitsa zinthu komanso kuti musankhe zinthu mwanzeru, zomwe zingathandize kuti mudzakhale ndi banja losangalala?

Musanayambe Chibwenzi

Kodi Ndine Wokonzeka Kukhala Pachibwenzi?

Mfundo 5 zimene zingakuthandizeni kudziwa ngati muli wokonzeka kukhala pachibwenzi komanso kulowa m’banja

Kodi Kukopana Kuli Ndi Vuto?

Kodi kukopana n’kutani? N’chifukwa chiyani anthu ena amakopana? Kodi kukopana kuli ndi vuto?

Kodi N’kungocheza Kapena Kukopana?

Nkhani imene munthu wina angaione ngati yocheza, wina angaione ngati yomukopa. Mungatani kuti muzipewa kutumiza mameseji olakwika?

Kodi Ndi Mnzanga Chabe Kapena Amandifuna?​—Gawo 1: Kodi Ndikuona Zizindikiro Zotani?

Nkhaniyi ingakuthandizeni kuti mudziwe ngati munthu amakukondani kapena akungofuna kukhala mnzanu chabe.

Kodi Ndi Mnzanga Chabe Kapena Amandifuna?—Gawo 2: Kodi Ndikumukopa?

Kodi mnzanuyu angaganize kuti mukumufuna chibwenzi? Zimene zingakuthandizeni.

Zofunika Kuganizira pa Nkhani ya Chibwenzi

Ngati mukukayikira kuti munthu winawake amakukondani, yankhani mafunso awa.

Musamapitirire Malire

Muzitumiza mameseji oyenera kwa anzanu amene si amuna kapena akazi anu.

Pamene Muli pa Chibwenzi

Kodi Ndi Chikondi Chenicheni Kapena Kungotengeka Maganizo?

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe tanthauzo la kutengeka maganizo ndiponso chikondi chenicheni.

Kodi Baibulo Limavomereza Kuti Mwamuna ndi Mkazi Azikhalira Limodzi Asanakwatirane?

Malangizo ochokera kwa Mulungu amatithandiza kudziwa zimene tingachite kuti tikhale ndi banja logwirizana ndipo anthu amene amatsatira mfundo zake zinthu zimawayendera bwino nthawi zonse.

Kodi a Mboni za Yehova Amatsatira Mfundo Ziti Zokhudza Kukhala pa Chibwenzi?

Kodi ndi bwino kukhala pa chibwenzi pongofuna kusangalala?

Chikondi Chenicheni

Mfundo za m’Baibulo zingathandize Akhristu posankha munthu woyenera kumanga naye banja, ndiponso zingawathandize kusonyezana chikondi chenicheni akakwatirana.

Kutha kwa Chibwenzi

Kukhala Pachibwenzi—Mbali Yachitatu: Kodi Ndithetse Chibwenzichi?

Kodi muyenera kupitiriza kukhala pachibwenzi ngati mukukayikira zinthu zina? Nkhaniyi ingakuthandizeni kusankha zoyenera kuchita.

Kodi Mungatani Ngati Chibwenzi Chatha?

N’chiyani chingakuthandizeni ngati chibwenzi chanu chatha?

Zomwe Zingakuthandizeni Ngati Chibwenzi Chatha

Mfundo zomwe zili mu zochitazi zikuthandizani kuti muzisangalalabe ngakhale kuti chibwenzi chatha.