Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

KODI BAIBULO LIMAPHUNZITSA CHIYANI?

Kodi Munthu Akafa Amapita Kuti? (Gawo 2)

N’chifukwa chiyani munthu oyambirira Adamu anafa? Kodi ndi cholinga cha Mulungu kuti anthu azifa? Fufuzani zimene Baibulo limanena. Sindikizani nkhaniyi kenako muyankhe mafunsowo.