Zoti Muchite Pophunzira Baibulo
Mulungu Amadana ndi Zinthu Zopanda Chilungamo
Mungaphunzire zambiri pa nkhani yokhudza Ahabu, Yezebeli, Naboti ndi Eliya. Koperani nkhani ya m’Baibuloyi, iwerengeni, ndipo muiganizire mozama n’kuona mmene ingakuthandizireni.