Kodi Tiyenera Kukondwerera Mabefide?
N’chifukwa chiyani timasankha kusakondwerera nawo mabefide? Tiyeni tione chifukwa chake komanso mmene tingayankhire ena akatifunsa.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Kodi Tiyenera Kukondwerera Mabefide?
Kodi ungathandize bwanji anthu ena kumvetsa chfukwa chake sumakondwerera mabefide?
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.