Munachitira Ine Amene
Tingathandize Akhristu odzodzedwa m’njira zambiri. Tiyeni tione zina mwa njirazi.
Makolo, werengani n’kukambirana ndi ana anu lemba la Mateyu 25:40.
Pangani dawunilodi n’kupulinta.
Mukaonera vidiyo yakuti, Munachitira Ine Amene, kambiranani ndi ana anu njira zosiyanasiyana zolalikirira, zakale ndi zamasiku ano zomwe, ndipo musankhepo njira imodzi yoti muifufuze pamodzi.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.