Posita: Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima
Positayi ingakukumbutse kuti Yehova akuthandiza kuti ukhale wolimba mtima ngati mtsikana wachiisiraeli uja.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima
N’chiyani chingakuthandizeni kuti muziuza ena zokhudza Yehova molimba mtima?
ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Kodi Yehova Angakuthandize Bwanji Kuti Ukhale Wolimba Mtima?
Yehova angakuthandize ngati mmene anathandizira kamtsikana ka ku Isiraeli.
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.