Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Yehova ndi Mnzanga Wapamtima

Yehova ndi Mnzanga Wapamtima

Yehova anapanga zinthu zokongola kuti anthufe tizisangalala chifukwa chakuti iye ndi Mnzathu. Kodi ungatchule zina mwa zinthu zomwe anapanga?

 

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

Khalani Bwenzi la Yehova (nyimbo zina)

Yehova Ndi Mnzanga Wapamtima

Sankhani Mulungu kuti akhale Bwenzi lanu lapamtima!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.