UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO April 2016
Maulaliki Acitsanzo
Maulaliki acitsanzo ogaŵila Galamukani! ndi buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa. Seŵenzetsani maulaliki acitsanzo amenewa kuti mukonze ulaliki wanu.
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Limbikitsani Ena ndi Mau Abwino
Anzake atatu a Yobu sanamutonthoze, koma anangoonjezela mavuto ake mwa kukamba mau oipa ndi kumuimba mlandu. (Yobu 16-20)
UMOYO WATHU WACIKRISTU
Mbali Yatsopano Yoyambitsila Makambilano
Yambani kukambilana nkhani za m’Baibulo poseŵenzetsa mbali yatsopano yakuti “Kodi Baibulo Limakamba Ciani?”
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Yobu Anapewa Maganizo Olakwika
Onani kusiyana pakati pa mabodza a Satana ndi mmene Yehova amationela. (Yobu 21-
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Yobu Anali Citsanzo Cabwino Pankhani Yosunga Umphumphu
Yobu anali wokonzeka kutsatila mfundo za Yehova za makhalidwe abwino, ndi kutengela cilungamo ca Mulungu. (Yobu 28-
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Bwenzi Lenileni Limapeleka Uphungu Wolimbikitsa
Tengelani mmene Elihu anacitila zinthu mwacikondi kwa mnzake Yobu. (Yobu 33-
KUONJEZELA LUSO LANU MU ULALIKI
Nchito Yogaŵila Tumapepala Toitanila Anthu ku Msonkhano Wacigawo
Zimene mufunika kudziŵa pamene muitanila anthu ku msonkhano wacigawo wa Mboni za Yehova. Yesezani maulaliki acitsanzo.
UMOYO WATHU WACIKRISTU
Zikumbutso za Msonkhano Wacigawo
Ganizilani mmene mungaonetsele ena cikondi pa msonkhano wacigawo.