Maulaliki Acitsanzo
GALAMUKANI!
Kugaŵila Cofalitsa: Ndakubweletselani Galamukani! iyi yatsopano.
Funso: Onani funso ili patsamba 2. Kodi muganiza bwanji?
Lemba: Luka 7:35
Nkhani iyi ifotokoza mmene mfundo imeneyi ilili yoona ponena za Baibulo.
GALAMUKANI!
Funso: Kodi muvomeleza kuti mau awa ndi ofunika kuwatsatila?
Lemba: Mat. 6:34
Kugaŵila Cofalitsa: [Pezani nkhani yakuti “Lingaliro la Baibulo—Nkhawa.”] Nkhani ino ionetsa mmene Baibulo lingatithandizile kulimbana ndi nkhawa.
Zimene Baibo Imaphunzitsa
Funso: Anthu amene amakhulupilila Mulungu amafuna kumuyandikila. Kodi mudziŵa kuti Baibulo limatilimbikitsa kuyandikila Mulungu?
Lemba: Yak. 4:8a
Kugaŵila Cofalitsa: Buku ili linapangidwa kuti litithandize kudziŵa zambili za Mulungu mwa kuseŵenzetsa Baibulo. [Fotokozani mfundo za m’nkhani 1 m’buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa.]
LEMBANI ULALIKI WANU
Onani maulaliki acitsanzo amene asonyezedwa kale kuti akuthandizeni kulemba ulaliki wanu.