CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YOBU 28-32
Yobu Anali Citsanzo Cabwino Pankhani Yosunga Umphumphu
Yobu anali wokonzeka kutsatila mfundo za Yehova za makhalidwe abwino
31:1
Yobu sanayang’ane mkazi wina momusilila, kupatulapo mkazi wake
Yobu anali citsanzo cabwino pocita zinthu ndi ena
31:13-15
Anali wodzicepetsa, wolungama, ndi wacifundo. Anali kuganizila anthu onse, kaya ndi olemela kapena osauka
Yobu anali wopatsa, osati wodzikonda
31:16-19
Anali kuthandiza anthu ovutika