UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO April 2017
Maulaliki a Citsanzo
Maulaliki a citsanzo oseŵenzetsa pogaŵila Galamukani! ndi mfundo yokhudza Ufumu wa Mulungu. Seŵenzetsani maulaliki a citsanzo pokonza ulaliki wanu.
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Lolani Kuti Yehova Aumbe Maganizo na Khalidwe Lanu
Woumba Wamkulu amaumba makhalidwe athu akuuzimu, koma tifunika kucita mbali yathu.
UMOYO WACIKHRISTU
Alandileni Bwino
Aliyense amene wabwela pa misonkhano ayenela kuonetsedwa cikondi. Kodi mungacite ciani kuti pa Nyumba ya Ufumu pakhale malo acikondi ndi aubwenzi?
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Kodi Muli na “Mtima Wodziŵa” Yehova?
Mu Yeremiya caputa 24, Yehova Mulungu anayelekezela anthu ndi nkhuyu. N’ndani anali monga nkhuyu zabwino, ndipo tingatengele bwanji citsanzo cawo?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Mukhoza Kulimbikitsa Mkhristu Wozilala
Ozilala amakhalabe amtengo wapatali kwa Yehova Mulungu. Tingawathandize bwanji kubwelela mumpingo?
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya
Yeremiya analosela kuti Yerusalemu adzasakazidwa. N’ciani cinam’thandiza kukhalabe wolimba mtima?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Nyimbo za Ufumu Zimathandiza Kukhala Wolimba Mtima
Kuimba nyimbo za Ufumu kunalimbikitsa Akhristu pamene anali mndende ya Sachsenhausen. Nyimbo zimenezi zingatilimbikitse tikamakumana na ziyeso.
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Yehova Ananenelatu za Pangano Latsopano
Kodi pangano latsopano lisiyana bwanji ndi pangano la Cilamulo, ndipo mapindu ake ni a muyaya m’njila yanji?