Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

April 17-23

YEREMIYA 25-28

April 17-23
  • Nyimbo 137 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya”: (10 min.)

    • Yer. 26:2-6—Yehova anauza Yeremiya kulengeza uthenga wa cenjezo (w09 12/1 peji 24 pala. 6)

    • Yer. 26:8, 9, 12, 13—Yeremiya sanayope adani ake pomuopseza (jr peji 21 pala. 13)

    • Yer. 26:16, 24—Yehova anateteza mneneli wake wolimba mtimawo (w09 12/1 peji 25 pala. 1)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yer. 27:2, 3—N’cifukwa ciani amithenga ocokela ku mitundu yosiyana-siyana anabwela ku Yerusalemu? Ndipo n’cifukwa ciani Yeremiya anawapangila magoli? (jr peji 27 pala. 21)

    • Yer. 28:11—Kodi Yeremiya anaonetsa bwanji kuzindikila pamene Hananiya anam’tsutsa? Nanga tingaphunzilepo ciani? (jr peji 187-188 mapa. 11-12)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Yer. 27:12-22

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 mineti kapena kucepelapo) T-36—Yalani maziko a ulendo wobwelelako.

  • Ulendo Wobwelelako: (4 mineti kapena kucepelapo) T-36—Yalani maziko a ulendo wobwelelako wotsatila.

  • Phunzilo la Baibo: (6 mineti kapena kucepelapo) lv peji 7 mapala. 4-5—Onetsani mmene mungafikile pamtima wophunzila.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU