YEREMIYA 25-28
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU |Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya
Yeremiya anacenjeza kuti Yerusalemu adzasakazidwa mofanana ndi mzinda wa Silo
26:6
-
Pa nthawi ina likasa la pangano, loimila Yehova, linali kusungidwila ku Silo
-
Yehova analola kuti Afilisiti alande likasalo, ndipo siinabwelelenso ku Silo
Ansembe, aneneli, ndi anthu onse anaopseza kuti adzamupha Yeremiya
26:8, 9, 12, 13
-
Anthu anam’gwila Yeremiya cifukwa colosela zakuti kacisi adzawonongedwa
-
Yeremiya sanaope ndi kuthaŵa
Yehova anam’teteza Yeremiya
26:16, 24
-
Yeremiya anakhalabe wolimba mtima, ndipo Yehova sanamusiye
-
Mulungu anacititsa Ahikamu wolimba mtima kuteteza Yeremiya
Yeremiya sanaleke kulengeza uthenga umene anthu anali kukwiya nawo cifukwa Yehova anali kumucilikiza na kumulimbikitsa kwa zaka 40