Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

April 3-9

YEREMIYA 17-21

April 3-9
  • Nyimbo 69 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • Lolani Kuti Yehova Aumbe Maganizo na Khalidwe Lanu(10 min.)

    • Yer. 18:1-4—Woumba amakhala na ulamulilo pa dothi lake (w99 4/1 peji 22 pala. 3)

    • Yer. 18:5-10—Yehova ali na ulamulilo pa anthu (it-2 peji 776 pala. 4)

    • Yer. 18:11—Lolani kuti Yehova akuumbeni (w99 4/1 peji 22 mapala. 4-5)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yer. 17:9—Kodi cinyengo ca mtima cingaonekele bwanji? (w01 10/15 peji 25 pala. 13)

    • Yer. 20:7—Kodi Yehova anaseŵenzetsa bwanji mphamvu zake pa Yeremiya na kum’putsitsa? (w07 3/15 peji 9 pala. 6)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Yer. 21:3-14

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Konzekelani Maulaliki a Mwezi Uno: (15 min.) Kukambilana “Maulaliki a Citsanzo.” Tambitsani vidiyo yake iliyonse, ndiyeno kambilanani zimene mwaphunzilapo. Limbikitsani onse kupanga maulendo obwelelako kwa anthu amene analandila kapepa kauthenga kakuti Kodi Ufumu wa Mulungu Ndi Ciani?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU