UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO April 2020
Makambilano Acitsanzo
Mpambo wa makambilano onena za colinga ca Mulungu kwa anthu, ndiponso mmene cidzakwanilitsidwila.
April 6-12
Kodi mudzakonzekeletsa bwanji mtima wanu kaamba ka Cikumbutso ca imfa ya Khristu?
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yakobo na Labani Acita Pangano la Mtendele
Kodi mungacite ciani kuti mukhalebe kapena kubwezeletsa mtendele na ena?
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Kodi Mukulimbikila kuti Mupeze Madalitso?
Kodi ndimwe ofunitsitsa kucita ciani kuti mulandile madalitso a Mulungu?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Kodi Cofunika Koposa kwa Ine N’ciani?
Kodi nchito imene mumagwila ionetsa kuti mumaika zinthu zotani patsogolo?
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Zotulukapo Zoopsa za Mayanjano Oipa
Kodi tingadziŵe bwanji ngati munthu wina ni bwenzi labwino kapena ayi?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Cotsani Milungu Yacilendo”
Kodi tingacite ciani kuti tikondweletse Yehova kuti tipewe kuvutitsidwa na ziŵanda?