April 20-26
GENESIS 32-33
Nyimbo 21 na Pemphelo
Mawu Oyamba (1 min.)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Kodi Mukulimbikila kuti Mupeze Madalitso?”: (10 min.)
Gen. 32:24—Yakobo anagwebana na mngelo (w03 8/15 25 ¶3)
Gen. 32:25, 26—Yakobo sanaleke kugwebana na mngeloyo kufikila atadalitsidwa (it-2 190)
Gen. 32:27, 28—Yakobo anadalitsidwa cifukwa ca kulimbikila kwake (it-1 1228)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)
Gen. 32:11, 13-15—Tingatengele bwanji khama la Yakobo pa nkhani yokhazikitsa mtendele? (w10 6/15 22 ¶10-11)
Gen. 33:20—N’cifukwa ciani Yakobo anacha guwa lansembe “Mulungu, Mulungu wa Isiraeli”? (it-1 980)
Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mbali ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 32:1-21 (th phunzilo 5)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Woyamba: (5 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi. Kenako funsani omvetsela mafunso aya: Kodi Elise wacita ciani kuti alalikile molondola komanso mokhulutilitsa? Kodi Elise na Morgan athandizana bwanji polalikila?
Ulendo Wobwelelako Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 12)
Ulendo Wobwelelako Woyamba: (5 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno chulani na kukambilana vidiyo yakuti Kodi Phunzilo la Baibulo Limacitika Bwanji? (koma musaitambitse) (th phunzilo 16)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Kodi Cofunika Koposa kwa Ine N’ciani?”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Sumikani Maganizo pa Zolinga Zauzimu.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 111 ¶10-21
Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)
Nyimbo 150 na Pemphelo