April 27–May 3
GENESIS 34-35
Nyimbo 28 na Pemphelo
Mawu Oyamba (1 min.)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Zotulukapo Zoopsa za Mayanjano Oipa”: (10 min.)
Gen. 34:1—Mobweleza-bweleza Dina anali kupita kukaceza na ana aakazi acikanani (w97 2/1 30 ¶4)
Gen. 34:2—Sekemu anagwilila Dina (lvs 124 ¶14)
Gen. 34:7, 25—Simiyoni na Levi anapha Sekemu pamodzi na mwamuna aliyense wa mumzindawo (w09 9/1 21 ¶1-2)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)
Gen. 35:8—Kodi Debora anali ndani? Nanga tingaphunzile ciani kwa iye? (it-1 600 ¶4)
Gen. 35:22-26—Tidziŵa bwanji kuti kukhala pa mzele wa makolo a Mesiya sikunadalile kukhala woyamba kubadwa? (w17.12 14)
Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mbali ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 34:1-19 (th phunzilo 5)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Waciŵili: (5 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi. Ndiyeno funsani omvetsela mafunso otsatilawa: Kodi Elise wayesetsa bwanji kum’fika pamtima mwininyumba? Kodi tingayambitse bwanji phunzilo la Baibo m’buku la Zimene Baibulo Ingatiphunzitse?
Ulendo Wobwelelako Waciŵili: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 13)
Phunzilo la Baibo: (5 min. olo kucepelapo) fg phunzilo 4 ¶6-7 (th phunzilo 14)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Cotsani Milungu Yacilendo”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti “Tsutsani Mdyelekezi”.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 112
Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)
Nyimbo 143 na Pemphelo