GENESIS 34-35
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU |Zotulukapo Zoopsa za Mayanjano Oipa
34:1, 2, 7, 25
Ngati maneba athu, anzathu a kunchito kapena a kusukulu ali na makhalidwe abwino, kodi zitanthauza kuti angakhale mabwenzi abwino? N’ciani cingatithandize kudziŵa ngati munthu wina ni bwenzi labwino kapena ayi?
-
Kodi kukhala nawo paubwenzi kudzanithandiza kulimbitsa ubale wanga na Yehova?
-
Kodi zokamba zawo zimaonetsa kuti cofunika kwambili kwa iwo n’ciani?—Mat. 12:34
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi mabwenzi anga amanilimbikitsa kukhala pa ubale wabwino na Yehova?’