Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

August 8-14

MASALIMO 92-101

August 8-14
  • Nyimbo 28 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (Mph. 3 kapena zocepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • Amabala Zipatso Ngakhale ni Okalamba”: (Mph. 10)

    • Sal. 92:12—Wolungama amabala zipatso zauzimu (w07 9/15-CN, tsa. 32; w06 7/15-CN, tsa. 13 ndime 2)

    • Sal. 92:13, 14—Okalamba angabale zipatso zauzimu ngakhale atakhala na thanzi lofooka (w14 1/1, tsa. 26 ndime 17; w04 5/15-CN, tsa. 12 ndime 9-10)

    • Sal. 92:15—Okalamba angalimbikitse ena mwa kuwafotokozela zimene aona paumoyo wawo (w04 5/15-CN, masa. 12-14 ndime 13-18)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (Mph. 8)

    • Sal. 99:6, 7—N’cifukwa ciani Mose, Aroni, na Samueli ni zitsanzo zabwino kwambili? (w15 7/15 tsa. 8 ndime 5)

    • Sal. 101:2—Kodi ‘kuyenda ndi mtima wosagaŵanika’ m’nyumba yathu kutanthauza ciani? (w05 11/1-CN, tsa. 24 ndime 14)

    • Kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno kwaniphunzitsa ciani za Yehova?

    • Ni mfundo ziti pa kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ningaseŵenzetse mu ulaliki?

  • Kuŵelenga Baibulo: (Mph. 4 kapena zocepelapo) Sal. 95:1–96:13

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 2 kapena zocepelapo) g16. Na. 4 nkhani ya pacikuto—Yalani maziko a ulendo wobwelelako.

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4 kapena zocepelapo) g16. Na. 4 nkhani ya pacikuto—Yalani maziko a ulendo wina wobwelelako.

  • Phunzilo la Baibulo: (Mph. 6 kapena zocepelapo) bh masa. 161-162 ndime 18-19—Thandizani wophunzila kuona mmene angaseŵenzetsele mfundo za m’nkhani imeneyo.

UMOYO WATHU WACIKHIRISTU

  • Nyimbo 90

  • Acikulile—Ndinu Ofunika Kwambili (Sal. 92:12-15): (Mph. 15) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti: AcikulileNdinu Ofunika Kwambili. (Pitani pa jw.org, ndi kuona polemba kuti MABUKU > MAVIDIYO.) Ndiyeno pemphani omvela kuti akambe zimene aphunzilapo. Limbikitsani acikulile kuti aziuzako acicepele zinthu zimene iwo adziŵa. Limbikitsaninso acicepele kuti azifunsila kwa acikulile akafuna kupanga zosankha zofunika kwambili pa umoyo wawo.

  • Phunzilo la Baibulo la Mpingo: (Mph. 30) ia mutu 21 ndime 13-22, ndi kubwelelamo pa tsa. 186

  • Kubwelelamo ndi Kuchulako za Mlungu Wotsatila (Mph. 3)

  • Nyimbo 29 na Pemphelo