MASALIMO 92-101
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU |Amabala Zipatso Ngakhale ni Okalamba
92:12
Mitengo ina ya kanjedza imakhala zaka zoposa 100, ndipo imabalabe zipatso
Acikulile amabala zipatso zauzimu mwa . . .
92:13-15
-
kupemphelela ena
-
kuphunzila Baibulo
-
kupezeka pamisonkhano na kuyankhapo
-
kuuzako ena zinthu zimene adziŵa
-
kulalikila modzipeleka