Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Maulaliki a Citsanzo

Maulaliki a Citsanzo

GALAMUKANI!

Funso: Kodi muganiza kuti munthu angapindule bwanji ngati ayesetsa kuleka zizoloŵezi zoipa?

Lemba: Mlal. 7:8a

Cogaŵila: Nkhani izi zifotokoza mfundo za m’Baibulo zimene zingathandize anthu kusintha zizoloŵezi zawo kuti akhale na umoyo wabwino.

GALAMUKANI!

Funso: Zinthu pa umoyo zimasintha-sintha. Muganiza kuti n’ciani cingatithandize kukhalabe acimwemwe ngati zinthu zina zasintha pa umoyo wathu?

Lemba: Mlal. 7:10

Cogaŵila: [Aonetseni nkhani imene iyambila patsamba 10.] Nkhani iyi ifotokoza mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize ngati zinthu zina zasintha pa umoyo wathu.

MVETSELANI KWA MULUNGU KUTI MUKHALE NDI MOYO WAMUYAYA

Funso: Aliyense wa ife ali na dzina. Ngakhale acibale athu ndi anzathu naonso ali na maina. Nanga Mulungu dzina lake n’ndani?

Lemba: Sal. 83:18

Cogaŵila: Kabuku aka kafotokoza zinthu zina zambili zimene Baibulo imakamba ponena za Mulungu. [Afotokozeleni mwacidule zimene zili pa masamba 6 ndi 7.]

KONZANI ULALIKI WANU

Funso:

Lemba:

Cogaŵila: