Akuimba nyimbo pa kulambila kwa pabanja ku South Africa

UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO December 2018

Makambilano Acitsanzo

Makambilano otsatizana-tsatizana ofotokoza colinga ca moyo na lonjezo la Mulungu la m’tsogolo.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Wozunza Akhristu Mwankhaza Akhala Mlaliki Wokangalika

Ngati mumaphunzila Baibo koma simunabatizike, kodi mudzatengela citsanzo ca Saulo mwa kucitapo kanthu mwamsanga pa zimene mumaphunzila?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Paulo na Baranaba Apanga Ophunzila Kumadela Akutali

Ngakhale kuti Paulo na Baranaba anatsutsidwa mwamphamvu, anacita khama kuthandiza anthu ofatsa kukhala Akhristu.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuthandiza Anthu a “Maganizo Abwino” Kukhala Ophunzila

Kodi timagwila bwanji nchito na Yehova popanga ophunzila?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Cigamulo Cozikidwa pa Mawu a Mulungu

Tiphunzilapo ciani pa mmene nkhaniyi anaisamalila?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Muziimba Mosangalala Nyimbo Zotamanda Yehova

Kodi kuimba nyimbo za Ufumu kumatikhudza bwanji?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Tengelani Citsanzo ca Mtumwi Paulo Polalikila na Kuphunzitsa

Tingatengele bwanji citsanzo ca mtumwi Paulo pocita ulaliki wathu?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Mukhale Chelu ndi Kuyang’anila Gulu Lonse la Nkhosa”

Akulu amadyetsa nkhosa, kuziteteza na kuzisamalila. Amakumbukila kuti nkhosa iliyonse inagulidwa na magazi a mtengo wapatali a Khristu.