December 10-16
MACHITIDWE 12-14
Nyimbo 60 na Pemphelo
Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Paulo na Baranaba Apanga Ophunzila Kumadela Akutali”: (10 min.)
Mac. 13:2, 3—Yehova anasankha Saulo na Baranaba kuti acite nchito yapadela (bt peji 86 pala. 4)
Mac. 13:12, 48; 14:1—Kugwila kwawo nchito mwakhama, kunakhala na zotulukapo zabwino (bt peji 95 pala. 5)
Mac. 14:21, 22—Paulo na Baranaba analimbikitsa ophunzila atsopano (w14 9/15 peji 13 mapa. 4-5)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Mac. 12:21-23—Tiphunzilapo ciani pa zimene zinacitikila Herode? (w08 5/15 peji 32 pala. 7)
Mac. 13:9—N’cifukwa ciani Saulo anali ‘kuchedwanso Paulo’? (“Saulo, wochedwanso Paulo”, “Paulo” nwtsty mfundo zounikila)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Mac. 12:1-17
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo.
Vidiyo ya Kubwelelako Koyamba: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.
Nkhani: (6 min. olo kucepelapo) bt mape. 78-79 mapa. 8-9—Mutu: Tizipemphelela Okhulupilila Anzathu.
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuthandiza Anthu a ‘Maganizo Abwino’ Kukhala Ophunzila”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Yehova Mulungu Adzakuthandizani.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 45
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 55 na Pemphelo