Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 9-11

Wozunza Akhristu Mwankhaza Akhala Mlaliki Wokangalika

Wozunza Akhristu Mwankhaza Akhala Mlaliki Wokangalika

9:15, 16, 20-22

Saulo sanazengeleze kucitapo kanthu pa zimene anaphunzila. N’cifukwa ciani Saulo anacitapo kanthu pamene ena sanatelo? Cifukwa anali kuopa Mulungu koposa anthu, ndiponso anayamikila kwambili cifundo cimene Khristu anamuonetsa. Ngati mumaphunzila Baibo koma simunabatizike, kodi mudzatengela citsanzo ca Saulo mwa kucitapo kanthu mwamsanga pa zimene mumaphunzila?