Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Makambilano Acitsanzo

Makambilano Acitsanzo

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi tingapeze kuti malangizo otithandiza kukhala na umoyo wacimwemwe?

Lemba: Sal. 1:1, 2

Ulalo: Kodi kukonda ndalama na cuma kungasokoneze bwanji cimwemwe cathu?

○●○ ULENDO WOBWELELAKO WOYAMBA

Funso: Kodi kukonda ndalama na cuma kungasokoneze bwanji cimwemwe cathu?

Lemba: 1 Tim. 6:9, 10

Ulalo: Ni mapindu ati amene timapeza tikakhala acimwemwe?

○○● ULENDO WOBWELELAKO WACIŴILI

Funso: Ni mapindu ati amene timapeza tikakhala acimwemwe?

Lemba: Miy. 17:22

Ulalo: Kodi banja lingakhale bwanji lacimwemwe ngakhale pokumana na mavuto?