Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

February 29–March 6

ESITERE 1–5

February 29–March 6
  • Nyimbo 86 ndi Pemphelo

  • Mau Oyamba (Mph. 3 kapena zocepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • Esitere Analimba Mtima Kuteteza Anthu a Mulungu”: (Mph. 10)

    • [Onetsani Vidiyo Yofotokoza Buku la Esitere.]

    • Esitere 3:5-9—Hamani anafuna kupha anthu onse a Mulungu (ia tsa. 131 ndime 18-19)

    • Esitere 4:11–5:2—Esitere anali ndi cikhulupililo colimba cakuti sanaope kufa (ia tsa. 125 ndime 2; tsa. 134 ndime 24-26)

  • Kufufuza Cuma Cakuuzimu: (Mph. 8)

    • Esitere 2:15—Kodi Estere anaonetsa bwanji kuti anali wodzicepetsa ndi wodziletsa? (w06 CN 3/1 tsa. 9 ndime 8)

    • Esitere 3:2-4—N’cifukwa ciani Moredekai anali kukana kugwadila Hamani? (ia tsa. 131 ndime 18)

    • Kodi kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno kundiphunzitsa ciani za Yehova?

    • Ndi mfundo ziti pa kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingagwilitsile nchito mu ulaliki?

  • Kuŵelenga Baibulo: Esitere 1:1-15 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

KUONJEZELA LUSO LANU MU ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 2 kapena zocepelapo) Gaŵilani kabuku ka mutu wakuti Mvetselani kwa Mulungu. Ndiyeno yalani maziko a ulendo wobwelelako

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4 kapena zocepelapo) Citani citsanzo coonetsa wofalitsa akucita ulendo wobwelelako kwa munthu amene analandila kabuku ka mutu wakuti Mvetselani kwa Mulungu. Kambilanani tsamba 2 ndi 3 ndi kuyala maziko a ulendo wotsatila.

  • Phunzilo la Baibulo: (Mph. 6 kapena zocepelapo) Citani citsanzo coonetsa mmene mungacititsile phunzilo la Baibulo mwa kugwilitsila nchito kabuku ka mutu wakuti, Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya, tsamba 4 ndi 5 kwa mwininyumba amene analandila kabuku kakuti Mvetselani kwa Mulungu pa ulendo woyamba. (km 7/12 tsa. 2-3 ndime 4)

UMOYO WATHU WACIKRISTU

  • Nyimbo 71

  • Zosoŵa za pampingo: (Mph. 10)

  • Kodi Mukupindula Bwanji ndi Makonzedwe Atsopano a Msonkhano komanso Kabuku ka Msonkhano?: (Mph. 5) Nkhani yokambilana. Pemphani omvela kufotokoza mmene apindulila ndi makonzedwe atsopano a msonkhano wa mkati mwa mlungu. Limbikitsani onse kuti azikonzekela bwino msonkhanowu kuti azipindula kwambili.

  • Phunzilo la Baibulo la Mpingo: ia mutu 10 ndime 1-11, ndi bokosi pa tsa. 86 (Mph. 30)

  • Kubweleza Mfundo Zimene Taphunzila ndi Kufotokoza Zomwe Tidzaphunzila Mlungu Wamaŵa. (Mph. 3)

  • Nyimbo 113 ndi Pemphelo