UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO February 2018
Makambilano a Citsanzo
Makambilano ozikidwa pa mafunso akuti: Kodi Baibo ikali yothandiza masiku ano? Kodi Baibo imagwilizana na sayansi? Kodi malangizo a m’Baibo ni othandiza?
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Fanizo la Tiligu ndi Namsongole
Kodi Yesu akukamba za ciani m’fanizo ili? Kodi wofesa, mdani, na okolola akuimila ndani?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Mafanizo a Ufumu na Tanthauzo Lake Kwa Ise
Yesu anaseŵenzetsa mafanizo osavuta kumva pophunzitsa mfundo zozama za coonadi. Ni mfundo zina ziti zimene tingaphunzile mu Mateyu caputa 13?
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Kudyetsa Anthu Ambili Mwa Kugwilitsila Nchito Anthu Ocepa
Yesu anauza ophunzila ake kuti adyetse khamu la anthu, ngakhale kuti anali cabe na mitanda isanu ya mkate na nsomba ziŵili. N’ciani cinacitika, nanga zitiphunzitsa ciani?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Uzilemekeza Atate Ako ndi Amayi Ako
Yesu anagogomeza lamulo lakuti uzilemekeza atate ako ndi amayi ako. Kodi lamulo ili lili na malile?
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Kodi Muli na Maganizo a Ndani?
Kodi tifunika kucita ciani kuti tikwanilitse cifunilo ca Mulungu? Yesu anakamba zinthu zitatu zimene zingatithandize kupewa maganizo olakwika.
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuseŵenzetsa Mafunso Mwaluso
Yesu anali kuwafunsa mafunso omvela ake powaphunzitsa mfundo zosiyana-siyana. Tingatengele bwanji luso lake la kaphunzitsidwe mu ulaliki?
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Muzisamala Kuti Musadzipunthwitse Kapena Kupunthwitsa Ena
Yesu anaseŵenzetsa mafanizo pofuna kuphunzitsa za kuopsa kwa kudzipunthwitsa kapena kupunthwitsa ena. N’ciani cingakhale copunthwitsa mu umoyo wanu?