February 12-18
MATEYU 14-15
Nyimbo 93 na Pemphelo
Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
“Kudyetsa Anthu Ambili Mwa Kugwilitsila Nchito Anthu Ocepa”: (10 min)
Mat. 14:16, 17—Ophunzila anali cabe na mitanda isanu ya mkate na nsomba ziŵili (w13 7/1 peji 21 pala. 2)
Mat. 14:18, 19—Yesu anadyetsa khamu la anthu mwa kuseŵenzetsa ophunzila ake (w13 7/1 peji 21 pala. 3)
Mat. 14:20, 21—Anthu masauzande anapindula na cozizwitsa ca Yesu (nwtsty mfundo younikila pa Mat. 14:21; w13 7/1 peji 21 pala. 1)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Mat. 15:7-9—N’cifukwa ciani tifunika kupewa kucita zacinyengo? (nwtsty mfundo younikila)
Mat. 15:26—Kodi Yesu ayenela kuti anatanthauza ciani pamene anaseŵenzetsa mau akuti “tiagalu”? (nwtsty mfundo younikila)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Mat. 15:1-20
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano a citsanzo.
Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Woyamba: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.
Nkhani: (6 min. olo kucepelapo) w15 9/15 mape. 19-20 mapa. 14-17—Mutu: Kuyang’anitsitsa Yesu Kudzalimbitsa Cikhulupililo Canu.
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Khala Bwenzi la Yehova—Kupanga Mabwenzi: (7 min.) Tambitsani vidiyo imeneyi. Pambuyo pake, itanani ana amene munasankha kuti abwele ku pulatifomu, na kuwafunsa mafunso aya: N’cifukwa ciani mufunika kupanga ubwenzi na anthu okonda Yehova? Nanga mungaphunzile ciani kwa iwo?
“Uzilemekeza Atate Ako ndi Amayi Ako”: (8 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo ya tukadoli yakuti Ningakambe Nawo Bwanji Makolo Anga?
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 8
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 148 na Pemphelo