Kodi Muli na Maganizo a Ndani?
-
Ngakhale kuti mwina Petulo anali kukamba ali na zolinga zabwino, Yesu sanazengeleze kumuwongolela pa kaganizidwe kake kolakwika.
-
Yesu anadziŵa kuti imeneyo siinali nthawi yakuti ‘adzikomele mtima.’ Mosakayikila, Satana ndiye anali kufuna kuti Yesu adzikomele mtima panthawi yovuta ngati imeneyo.
Yesu anachula zinthu zitatu zotithandiza kukwanilitsa cifunilo ca Mulungu. Kodi ciliconse ca zinthuzi citanthauza ciani?
-
Kudzikana wekha:
-
Kunyamula mtengo wako wozunzikilapo:
-
Kutsatila Yesu mosalekeza: