Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

February 5-11

MATEYU 12-13

February 5-11
  • Nyimbo 27 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • Fanizo la Tiligu ndi Namsongole”: (10 min.)

    • Mat. 13:24-26—Munthu wina anafesa mbewu zabwino m’munda mwake, ndiyeno mdani wake anafesa namsongole m’mundamo (w13 7/1 mape. 15-16 mapa. 2-3)

    • Mat. 13:27-29—Tiligu ndi namsongole zinakulila pamodzi mpaka nthawi yokolola (w13 7/1 peji 16 pala. 4)

    • Mat. 13:30—Pa nthawi yokolola, coyamba okolola anasonkhanitsa namsongole pamodzi, kenako anasonkhanitsa tiligu (w13 7/1 mape. 18-19 mapa. 10-12)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Mat. 12:20—Kodi tingatengele bwanji cifundo ca Yesu? (nwtsty mfundo younikila)

    • Mat. 13:25—Kodi n’zoona kuti kale anthu anali kufesa namsongole m’minda ya anthu ena? (w16.10 peji 32)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Mat. 12:1-21

CITANI KHAMA PA ULALIKI

UMOYO WATHU WACIKHRISTU