UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Mafanizo a Ufumu na Tanthauzo Lake Kwa Ise
Yesu anaseŵenzetsa mafanizo osavuta kumva pophunzitsa mfundo zozama za coonadi. Komabe, ni anthu odzicepetsa okha amene amamvetsetsa na kuseŵenzetsa zimene iye anaphunzitsa. (Mat. 13:10-15) Pa fanizo lililonse la Ufumu, yankhani mafunso otsatilawa: Kodi ningapindule bwanji na fanizoli? Nanga linganithandize bwanji mu umoyo wanga?
UFUMU WAKUMWAMBA ULI NGATI . . .
-
“kanjele ka mpilu.”—Mat. 13:31, 32. w14 12/15 peji 8 pala. 9.
-
“zofufumitsa.”—Mat. 13:33; w14 12/15 mape. 9-10 pala. 14-15.
-
“cuma” ndi “wamalonda woyendayenda.”—Mat. 13:44-46; w14 12/15 peji 10 pala. 18.