February 11-17
AROMA 4-6
Nyimbo 20 na Pemphelo
Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Mulungu Akuonetsa Cikondi Cake Kwa Ife”: (10 min.)
Aroma 5:8, 12—Yehova anationetsa cikondi “pamene tinali ocimwa” (w11 6/15 peji 12 pala. 5)
Aroma 5:13, 14—Ucimo na imfa zinalamulila monga mfumu (w11 6/15 peji 12 pala. 6)
Aroma 5:18, 21—Yehova anatumiza mwana wake kuti tilandile moyo (w11 6/15 mape. 12-13 mapa. 9-10)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Aroma 6:3-5—Kodi kubatizidwa “mu mgwilizano ndi Khristu Yesu” komanso kubatizidwa “mu imfa yake,” kukutanthauza ciani? (w08 6/15 peji 29 pala. 7)
Aroma 6:7—N’cifukwa ciani oukitsidwa sadzaweluzidwa mogwilizana na macimo amene anacita akalibe kufa? (w14 6/1 peji 11 pala. 1)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Aroma 4:1-15 (th phunzilo 10)
CITANI KHAMA PA ULALIKI]
Vidiyo ya Kubwelelako Koyamba: (4 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.
Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 4)
Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Mukayamba makambilano acitsanzo, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko amene anthu amakamba pokana kuwalalikila. Koma muyankheni mwaluso. (th phunzilo 6)
Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno gaŵilani cofalitsa cophunzitsila ca mu Thuboksi yathu. (th phunzilo 9)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Zofunikila za Mpingo: (15 min.)
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 54
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 97 na Pemphelo