February 4-10
AROMA 1-3
Nyimbo 88 na Pemphelo
Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
“Pitilizani Kuphunzitsa Cikumbumtima Canu”: (10 min.)
[Tambitsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Aroma.]
Aroma 2:14, 15—Munthu aliyense ali na cikumbumtima (lv peji 16 pala. 6)
Aroma 2:15—Tifunika kuphunzitsa cikumbumtima cathu kuti cizititsogolela bwino (lv mape. 17-18 mapa. 8-9)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Aroma 3:4—Kodi timalola bwanji ‘Mulungu kukhala wonena zoona’? (w08 6/15 peji 30 pala. 5)
Aroma 3:24, 25—Kodi “dipo lolipilidwa ndi Khristu Yesu” linaphimba bwanji “macimo amene anacitika kale”? (w08 6/15 peji 29 pala. 6)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Aroma 1:1-17 (th phunzilo 10)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa: (10 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Kukambilana Mwacibadwa, ndiyeno kambilanani phunzilo 2 m’kabulosha kakuti Kuphunzitsa.
Nkhani: (5 min. olo kucepelapo) w06 6/1 mape. 12-13—Mutu: Muziona Moyenela Zimene Simungakwanitse Kucita na Zimene Ena Sangakwanitse Kucita. (th phunzilo 7)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Kodi Mumawaona Makhalidwe Osaoneka a Mulungu?”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Zodabwitsa za Cilengedwe Zimaonetsa Ulemelelo wa Mulungu—Kuwala na Mitundu.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 53
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 142 na Pemphelo