Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

February 5-11

MASALIMO 1-4

February 5-11

Nyimbo 150 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Khalani ku Mbali ya Ufumu wa Mulungu

(Mph. 10)

[Tambitsani VIDIYO yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Masalimo.]

Maboma a anthu adzipanga okha kukhala adani a Ufumu wa Mulungu (Sal. 2:2; w21.09 15 ¶8)

Yehova akupatsa anthu onse mpata wakuti asankhe kukhala ku mbali ya Ufumu wake (Sal. 2:​10-12)

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndine wotsimikiza kusakhalila mbali pa ndale za dziko, ngakhale kuti zimenezi zinganibweletsele mavuto?’—w16.04 29 ¶11.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Sal. 1:4—Kodi anthu oipa ali ngati “mankhusu amene amauluzika ndi mphepo” m’lingalilo lotani? (it-1 425)

  • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutigaŵilako?

3. Kuŵelenga Baibo

(Mph. 4) Sal. 3:1–4:8 (th phunzilo 12)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kukamba Mwacibadwa—Mmene Filipo anacitila zimenezi

(Mph. 7) Kukambilana. Tambitsani VIDIYO yakuti kenako kambilanani lmd phunzilo 2 mfundo 1-2.

5. Kukamba Mwacibadwa—Tengelani Citsanzo ca Filipo

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 32

6. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

7. Phunzilo la Baibo la Mpingo

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 61 na Pemphelo