Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

January 1-7

YOBU 32-33

January 1-7

Nyimbo 102 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Mwa cifundo, Elihu akumvetsela pamene Yobu akufotokoza mmene akumvela

1. Tonthozani Omwe Ali na Nkhawa

(Mph. 10)

Khalani mabwenzi kwa ena (Yobu 33:1; it-1 710)

Khalani acifundo m’malo mowaweluza (Yobu 33:​6, 7; w14 6/15 25 ¶8-10)

Monga Elihu anacitila, yambani mwamvetsela na kuganizilapo musanalakhule (Yobu 33:​8-12, 17; w20.03 23 ¶17-18; onani cithunzi pacikuto)

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Yobu 33:25—Kodi vesiyi itithandiza bwanji kusamada nkhawa kwambili na maonekedwe athu tikayamba kukalamba? (w13 1/15 19 ¶10)

  • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zomwe mungakonde kutigaŵilako?

3. Kuŵelenga Baibo

(Mph. 4) Yobu 32:​1-22 (th phunzilo 12)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kambilanani pa Zokhudza Munthuyo—Mmene Yesu Anacitila Zimenezi

(Mph. 7) Kukambilana. Tambitsani VIDIYO yakuti kenako kambilanani lmd phunzilo 1 mfundo 1-2.

5. Kambilanani pa Zokhudza Munthuyo—Tengelani Yesu

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 116

6. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

7. Phunzilo la Baibo la Mpingo

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 54 na Pemphelo