January 13-19
MASALIMO 135-137
Nyimbo 2 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)
1. “Ambuye Wathu Ndi Wamkulu Kuposa Milungu Ina Yonse”
(Mph. 10)
Yehova waonetsa kuti ali na mphamvu zolamulila cilengedwe conse (Sal. 135:5, 6; it-2-E 661 ¶4-5)
Iye amateteza anthu ake (Eks. 14:29-31; Sal. 135:14)
Amatithandiza tikafooka (Sal. 136:23; w21.11 6 ¶16)
2. Kufufuza Cuma Cauzimu
(Mph. 10)
Sal. 135:1, 5—N’cifukwa ciyani mawu akuti “Ya” amaseŵenzetsedwa kaŵili-kaŵili m’Baibo? (it-1-E 1248)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?
3. Kuŵelenga Baibo
(Mph. 4) Sal. 135:1-21 (th phunzilo 11)
4. Kuyambitsa Makambilano
(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Patsanani mafoni namba na munthu amene waonetsa cidwi. (lmd phunzilo 2 mfundo 4)
5. Kubwelelako
(Mph. 4) KU NYUMBA NA NYUMBA. Muitanileni ku misonkhano. (lmd phunzilo 9 mfundo 4)
6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupilila
(Mph. 5) Citsanzo. ijwfq nkhani 7—Mutu: Kodi Mboni za Yehova ni Akhristu? (th phunzilo 12)
Nyimbo 10
7. Zofunikila za Mpingo
(Mph. 15)
8. Phunzilo la Baibo la Mpingo
(Mph. 30) bt mutu 21 ¶1-7, bokosi pa tsa. 166